LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 5/13 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 13
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MAY 13
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 5/13 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa May 13

MLUNGU WA MAY 13

Nyimbo 4 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 23 ndime 1-8 ndi bokosi patsamba 180 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Yohane 5–7 (Mph. 10)

Na. 1: Yohane 6:22-40 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi N’cifukwa Ciani Zinali Zoyenela Kuti Dipo Lipelekedwe M’njila Imene Linapelekedwela?—rs tsa. 122 ndime 6–tsa. 123 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingatsatile Bwanji Mfundo Yopezeka pa Numeri 15:37-40? (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 126

Mph. 10: Zogaŵila za mu May ndi June. Nkhani. Mwacidule fotokozani cifukwa cake tumapepala tumenetu tudzakopa cidwi ca anthu a m’gawo lanu. Citani citsanzo cosonyeza mmene mungagaŵile kapepala kamodzi kapena tuŵili pocita ulaliki wa nyumba ndi nyumba.

Mph. 10: Tiphunzilapo Ciani? Kukambilana. Ŵelengani Mateyu 5:11, 12 ndi Mateyu 11:16-19 ndipo kambilanani mmene malembawa angatithandizile mu utumiki.

Mph. 10: “N’ciani Cimatisonkhezela Kulalikila?” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo 91 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani