LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 6/13 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 24

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 24
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JUNE 24
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 6/13 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa June 24

MLUNGU WA JUNE 24

Nyimbo 123 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 25 ndime 1 mpaka 7, bokosi pa tsamba 199 ndi 200 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Machitidwe 8 mpaka 10 (Mph. 10)

Kubweleza za M’sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 93

Mph. 10: “Kambilanani Nkhani Imodzi, koma Gaŵilani Magazini Onse Aŵili.” Nkhani. Pambuyo pankhani, onetsani mmene mungayambitsile phunzilo pa Ciŵelu coyamba mu July, mwa kugwilitsila nchito ulaliki wacitsanzo amene ali patsamba 4.

Mph. 10: Nchito Yathu Sidzapita Pacabe. (Aheb. 6:10) Nkhani yokambilana yocokela mu Nsanja ya Olonda ya February 15, 2012, masamba 8-9. Pemphani omvela kuti akambepo zimene aphunzila.

Mph. 10: Zogaŵila za mu July ndi August. Nkhani. Mwacidule kambilanani nkhani zimene zipezeka m’kabuku kamene mudzagaŵila. Citani citsanzo coonetsa mmene mungagaŵilile tumabuku tuŵili. Citsanzo cimodzi cikhale ca mmene mungagaŵilile kabuku ka Uthenga Wabwino, mwa kugwilitsila nchito maulaliki acitsanzo ali patsamba 4 kapena opezeka mu Utumiki Wathu wa Ufumu wa March 2013.

Nyimbo 129 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani