LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 7/13 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 22

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 22
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JULY 22
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 7/13 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa July 22

MLUNGU WA JULY 22

Nyimbo 22 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 26 ndime 9-15 ndi bokosi patsamba 208 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Machitidwe 22–25 (Mph. 10)

Na. 1: Machitidwe 22:17-30 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: N’cifukwa Ciani Tinganene Kuti Sitili Mbali ya Dziko Ngakhale Kuti Timakhala M’dzikoli?—Yoh. 17:15, 16 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi N’zotheka Kuti Akristu Apite Kumwamba ndi Matupi Ao Enieni?—rs tsa. 214 ndime 4-tsa. 215 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 41

Mph. 10: “Mvetselani ndi Kuphunzila.” Mafunso ndi Mayankho.

Mph. 10: “Khalidwe Limene Limalemekeza Mulungu.” Mafunso ndi Mayankho. Kambilananinso “Zikumbutso za Msonkhano wa Cigawo wa 2013.”

Mph. 10: “Tengelani Citsanzo kwa Aneneli—Yoweli.” Mafunso ndi Mayankho.

Nyimbo 95 Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani