LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/13 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 21

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 21
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA OCTOBER 21
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 10/13 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa October 21

MLUNGU WA OCTOBER 21

Nyimbo 33 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jl phunzilo 14 mpaka 16 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: 1 Atesalonika 1 mpaka 2 Atesalonika 3 (Mph. 10)

Na. 1: 1 Atesalonika 2:9-20 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Tingaphunzile Ciani pa Zinthu Zabwino Komanso Zoipa Zimene Solomo Anacita?—Aroma 15:4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Baibo Imati Ciani pa Nkhani Yakuti Zipembedzo Zizicitila Zinthu Limodzi?—rs tsa. 86 ndime 1 mpaka tsa. 87 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 125

Mph. 15: Kodi Tiphunzilapo Ciani? Kukambilana. Ŵelengani Maliko 1:40-42, Maliko 7:32-35, ndi Luka 8:43-48 ndipo kambilanani mmene malembawa angatithandizile mu utumiki.

Mph. 15: “Njila Zocitila Kulambila kwa Pabanja.” Mafunso ndi mayankho. Pokambilana ndime 3, pemphani makolo ndi ana kuti afotokoze colinga ca kulambila kwa pabanja. Pokambilana ndime 4, pemphani omvela kuti afotokoze mmene aseŵenzetsela zinthu zosiyana-siyana kuti kulambila kwao kwa pabanja kukhale kosangalatsa kwa aliyense.

Nyimbo 88 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani