LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/13 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 2

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 2
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 2
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 11/13 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa December 2

MLUNGU WA DECEMBER 2

Nyimbo 123 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jr mutu 1 ndime 8 mpaka 14 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: 1 Petulo 1 mpaka 2 Petulo 3 (Mph. 10)

Na. 1: 1 Petulo 2:18 mpaka 25 ndi 3:1-7 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Cipembedzo Coona Cimaphunzitsa Zimene Baibo imanena Komanso Cimadziŵitsa Anthu Dzina la Mulungu—rs tsa. 89 ndime 3-4 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani Timakhulupilila Kuti Yesu Ndi Mesiya?—Luka 24:44; Agal. 4:4 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 116

Mph. 5: Kuyambitsa Maphunzilo a Baibo pa Ciŵelu Coyamba. Nkhani. Limbikitsani onse kutengako mbali mukuyambitsa maphunzilo a Baibo pa Ciŵelu coyamba mu December. Mwacidule citani citsanzo coonetsa mmene tingacitile zimenezi mwakugwilitsila nchito nkhani ili kucikuto cakumapeto kwa Nsanja ya Mlonda.

Mph. 15: Kodi munaziyesapo? Kukambilana. Mwacidule fotokozani mfundo za mu Utumiki Wathu wa Ufumu m’nkhani za posacedwapa izi: “Colinga ca Webusaiti Yathu Ndi Kuthandiza Ife ndi Anthu Ena” (km 12/12), ndi yakuti “Ndani Angacite Nazo Cidwi Izi?” (km 5/13). Pemphani omvela kuti afotokoze mmene aphindulila ndi mfundo zili m’nkhani zimenezi.

Mph. 10: Zosoŵa za pampingo.

Nyimbo 12 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani