LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/13 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 30

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 30
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 30
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 12/13 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa December 30

MLUNGU WA DECEMBER 30

Nyimbo 126 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jr mutu 2 ndime 14-19, ndi bokosi patsamba 25 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Chivumbulutso 15-22 (Mph. 10)

Kubweleza za m’Sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 43

Mph. 10: “Athandizeni kuti ‘Akhazikike m’Cikhulupililo.’” Nkhani. Ndiyeno, citani citsanzo cacidule ca mmene tingayambitsile phunzilo pogwilitsila nchito magazini pa Ciŵelu coyamba mu January. Limbikitsani onse kutengako mbali.

Mph. 10: Thandizani Mwana Wanu Kukhala Wofalitsa. Nkhani yozikidwa m’buku la Gulu patsamba 82, ndime 1 ndi 2. Funsani kholo la citsanzo cabwino limene mwana wake ndi wofalitsa wosabatizika. Kodi anathandiza bwanji mwana wake kuti ayenelele kukhala wofalitsa?

Mph. 10: Ndingacitenso Mantha Ndi Ndani? (Aheberi 13:5, 6) NKhani yokambilana yocokela mu Nsanja ya Olonda ya July 15, 2012 masamba 24-25, ndime 10-12. Pemphani omvela kuti afotokoze zimene aphunzilapo.

Nyimbo 119 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani