LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/13 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 23

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 23
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 23
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 12/13 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa December 23

MLUNGU WA DECEMBER 23

Nyimbo 127 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jr mutu 2 ndime 7-13, ndi bokosi patsamba 20 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Chivumbulutso 7–14 (Mph. 10)

Na. 1: Chivumbulutso 9:1-21 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Akristu Angasonyeze Bwanji Kuti Ndi Oceleza?—Aheb. 13:2 (Mph. 5)

Na. 3: Akristu a mu Cipembedzo Coona Amakondana Komanso Sakhala Mbali ya Dziko—rs tsa. 90 ndime 2-3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 124

Mph. 10: Cogaŵila mu January ndi February. Nkhani yokambilana. Kambilanani buku limene mudzagaŵila, ndipo khalani ndi zitsanzo ziŵili zosonyeza mmene mungagaŵilile bukulo.

Mph. 10: Acinyamata, Kodi Mudzacitako Upainiya Wothandiza Paholide? Nkhani. Fotokozani mwacidule ndime 1 patsamba 113 m’buku la Gulu. Chulani ziyeneletso za upainiya wothandiza. Ndiyeno funsani wofalitsa mmodzi kapena aŵili amene anacitako upainiya wothandiza pamene anali paholide. Limbikitsani acinyamata kuti akaciteko upainiya wothandiza akatsekela sukulu.

Mph. 10: Tiphunzilapo Ciani. Makambilano ocokela mu Nsanja ya Mlonda ya October 15, 2013, patsamba 20. Pemphani wofalitsa mmodzi kapena aŵili kuti afotokoze mwacidule mmene akhalila acipambano pa mavuto a tsiku ndi tsiku

Nyimbo 46 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani