LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 2/14 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 10

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 10
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA FEBRUARY 10
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 2/14 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa February 10

MLUNGU WA FEBRUARY 10

Nyimbo 57 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 4 ndime 9 mpaka 14 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Genesis 25-28 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 25:19-34 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Anthu Oukitsidwa Kuti Akalamulile ndi Kristu Adzakhala Ngati Iyeyo—rs tsa. 109 ndime 4-8 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Yehova Amaiona Bwanji Nkhani Yopembedza Mafano?—bh tsa. 154-156 ndime 1-5 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 94

Mph. 15: Kodi Tiphunzilapo Ciani? Kukambilana. Lemba la Yohane 4:6-26 liŵelengedwe. Kambilanani mmene nkhani imeneyi ingatithandizile mu ulaliki.

Mph. 15: “Kuongolela Luso Lathu mu Ulaliki—Tizilemba Tikapeza Anthu Acidwi.” Kukambilana. Pokambilana kadontho kalikonse pansi pa kamutu kakuti “Mmene Tizicitila,” pemphani omvela kuti afotokoze cifukwa cake malingalilo amenewa ndi othandiza kwambili.

Nyimbo 98 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani