LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 5/14 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 26

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 26
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MAY 26
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 5/14 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa May 26

MLUNGU WA MAY 26

Nyimbo 60 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 9 ndime 1 mpaka 7 (Mph. 30)

Sukulu ya ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Ekisodo 34-37 (Mph. 10)

Na. 1: Ekisodo 34:1-16 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Cifukwa Cimene Malamulo Onse Amakhalidwe Abwino Sanacotsedwe Pamene Malamulo Khumi Anacotsedwa—rs tsa. 349 ndime 1-2 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani Tiyenela Kuphunzitsa Cikumbumtima Cathu?—(Iv tsa. 17-19 ndime 8 mpaka 11¶ (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 32

Mph. 10: Kuyambitsa Maphunzilo a Baibulo pa Ciŵelu Coyamba. Kukambilana. Pemphani omvela kuti afotokoze zimene anakumana nazo poyambitsa maphunzilo a Baibulo pa Ciŵelu coyamba ca mwezi. Citani citsanzo coonetsa mmene tingayambitsile phunzilo la Baibulo pa Ciŵelu coyamba mu June, pogwilitsila nchito ulaliki wacitsanzo umene uli pa tsamba 4. Limbikitsani onse kuti azitengako mbali.

Mph. 10: Kupilila Mazunzo Kumathandiza Kupeleka Umboni Wabwino (Luka 21:12, 13) Kukambilana kocokela mu Nsanja ya Olonda ya May 15, 2013 tsamba 11, ndime 12 mpaka 14. Pemphani omvela kuti afotokoze zimene aphunzilapo.

Mph. 10: Bokosi la Mafunso. Nkhani yokambidwa ndi mkulu. Pemphani acikulile kuti afotokoze mmene apindulila cifukwa cophunzitsidwa mozama coonadi ca m’Baibulo ndi makolo ao.

Nyimbo 88 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani