LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 5/14 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 2

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 2
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JUNE 2
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 5/14 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa June 2

MLUNGU WA JUNE 2

Nyimbo 134 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 9 ndime 9 mpaka 13 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Ekisodo 38-40 (Mph. 10)

Na. 1: Ekisodo 40:20-38 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Sabata Limatanthauza Ciani kwa Akristu?—rs tsa. 349; yakonzedwanso: w11 7/15 tsa. 28 ndime 16-17 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingaphunzile Ciani pa Nkhani za Anthu Amene Anaukitsidwa Zopezeka m’Baibulo?—(bh tsa. 70-71 ndime 11 mpaka 15 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 115

Mph. 10: Kugaŵila Magazini mu June. Kukambilana. Yambani ndi citsanzo ca mmene mungagaŵilile magazini, pogwilitsila nchito maulaliki aŵili acitsanzo amene ali pa tsamba lino. Ndiyeno kambilananinso maulaliki acitsanzo amenewo kuyambila poyamba mpaka pa mapeto. Mwacidule malizani mwa kulimbikitsa onse kuti aziwadziŵa bwino magazini ndipo azitengako mbali mosangalala powagaŵila kwa ena.

Mph. 10: Zosoŵa za pampingo.

Mph. 10: Tinacita Zotani? Kukambilana. Pemphani omvela kuti akambe mapindu amene apeza pogwilitsila nchito mfundo za m’nkhani yakuti “Kuongolela Luso Lathu mu Ulaliki—Kukonzekela Mau Athu Oyamba.” Pemphani omvela kuti afotokoze zocitika zolimbikitsa za mu utumiki.

Nyimbo 44 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani