LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 6/14 tsa. 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 30

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 30
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JUNE 30
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 6/14 tsa. 7

Ndandanda ya Mlungu wa June 30

MLUNGU WA JUNE 30

Nyimbo 5 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 10 ndime 14 mpaka 19 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Levitiko 14-16 (Mph. 10)

Kubweleza za M’sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 58

Mph. 10: “Mufunika Kubwelelako Mwamsanga.” Nkhani. Pambuyo pake, citani citsanzo coonetsa mmene tingayambitsile maphunzilo a Baibulo mu July pa Ciŵelu coyamba pogwilitsila nchito maulaliki acitsanzo amene ali pa tsamba 8.

Mph. 20: Phunzilo Laumwini Limathandiza Kuti Tikhale Atumiki Olimba. Kukambilana kozikidwa m’buku la sukulu ya utumiki, tsamba 27-32. Funsani mafunso wofalitsa amene amadziŵika ndi zizoloŵezi zabwino za kuphunzila.

Nyimbo 69 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani