LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 5/15 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 18

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 18
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MAY 18
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 5/15 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa May 18

MLUNGU WA MAY 18

Nyimbo 50 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 9 ndime 21-24, ndi bokosi pa tsa. 96 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 2 Samueli 9-12 (Mph. 8)

Na. 1: 2 Samueli 10:13–11:4 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Benaya—Mutu: Khalani Olimba Mtima Komanso Okhulupilika—(w05 5/1 tsa. 15 ndime 11) (Mph. 5)

Na. 3: Tingakhale ndi Ciyembekezo Cotani Kaamba ka Anthu Akufa?—(igw-CIN tsa. 19 ndime 1-3) (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: Thandizani anthu a mitundu yonse kudziŵa coonadi molondola.—1 Tim. 2:3, 4.

Nyimbo 73

Mph. 10: Mmene Paulo Anathandizila Agiriki Kudziŵa Coonadi Molondola. Kukambilana. Ŵelengani Machitidwe 17:22-31. Ndiyeno kambilanani mmene nkhaniyi ingatithandizile mu ulaliki.

Mph. 20: Yehova Adzakuthandizani Kukhala Olimba Mtima. Kukambilana. Onelelani vidiyo yakuti, Jehovah Will Help You Be Bold [Yehova Adzakuthandizani Kukhala Olimba Mtima]. (Pitani pa jw.org, ndi kuona polemba kuti BIBLE TEACHINGS > CHILDREN.) Pemphani omvela kuti akambe zimene aphunzila m’vidiyo imeneyi. Ngati n’zosatheka kuonelela vidiyoyi, kambilanani nkhani ya mu Nsanja ya Olonda ya February 15, 2012 tsa. 12 ndime 11. Pemphani ana a sukulu kuti afotokoze zimene zawathandiza kukhala olimba mtima polalikila kwa ana a sukulu anzao ndi aphunzitsi. Mwana wa sukulu acite citsanzo ca cocitikaco pamene anali kulalikila kusukulu.

Nyimbo 60 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani