LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 5/15 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 25

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 25
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MAY 25
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 5/15 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa May 25

MLUNGU WA MAY 25

Nyimbo 56 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 10 ndime 1-7, (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 2 Samueli 13-15 (Mph. 8)

Na. 1: 2 Samueli 13:34–14:7 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Baibulo Limakamba Ciani za Nchito?—(igw-CIN tsa. 20 ndime 1-3) (Mph. 5)

Na. 3: Bezaleli—Mutu: Mzimu wa Yehova Umathandiza Atumiki Ake pa Nchito Iliyonse Yabwino—(w11 12/15 tsa. 19 ndime 6-7) (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: Thandizani anthu a mitundu yonse kudziŵa coonadi molondola.—1 Tim. 2:3, 4.

Nyimbo 121

Mph. 10: Kufunsa Mafunso Woyang’anila Kagulu ka Ulaliki. Kodi mumagwila nchito yotani pa udindo wanu? Kodi mumakwanitsa bwanji kusamalila ofalitsa a m’kagulu kanu ndi kuwathandiza mu ulaliki? N’cifukwa ciani ofalitsa afunika kukudziŵitsani ngati asintha nambala ya foni kapena malo okhala? N’cifukwa ciani akulu amakonza zakuti kagulu ka ulaliki kazikumana pakokha pokonzekela ulaliki m’malo mocitila pa malo amodzi?

Mph. 20: “Thandizani Anthu Akhungu Kuphunzila za Yehova.” Mafunso ndi mayankho. Mucitenso citsanzo.

Nyimbo 96 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani