LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 7/15 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 13
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JULY 13
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 7/15 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa July 13

MLUNGU WA JULY 13

Nyimbo 75 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 27 ndime 10-18 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Mafumu 9-11 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Mafumu 9:24–10:3 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Mungacepetse Nkhawa Mwa Kuphunzila Mau a Mulungu—igw-CIN tsa. 24 ndime 4–tsa. 25 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Koresi—Mutu: Mau a Mulungu Amakwanilitsidwa Nthawi Zonse—w14 5/1 tsa. 5 ndime 2 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Pitani mukaphunzitse anthu.”—Mat. 28:19, 20.

Nyimbo 17

Mph. 10: Pitani Mukaphunzitse Anthu. Nkhani yozikidwa pa lemba la mwezi. Fotokozaninso mfundo za m’buku la “Bwera Ukhale Wotsatira Wanga,” masamba 87-89. Mwacidule, chulani nkhani za mu Msonkhano wa Nchito zamwezi uno, ndipo fotokozani mmene zikugwilizanilana ndi lemba la mwezi.

Mph. 10: Anali Wokonzeka Kuyambitsa Phunzilo la Baibulo. Nkhani yokambilana yocokela mu Buku la Pacaka la 2015, tsamba 55, ndime 1, mpaka tsamba 56, ndime 1 ndi tsamba 69, ndime 2-5. Ndiyeno pemphani omvela kuti akambe zimene aphunzilapo.

Mph. 10: “Ikani Maganizo Anu pa Nchito Yophunzitsa Anthu.” Mafunso ndi mayankho. Mwacidule funsani mafunso ofalitsa mmodzi kapena aŵili amene amacita bwino poyambitsa ndi kucititsa phunzilo la Baibulo. Ndi mapindu otani amene apeza pothandiza winawake kuphunzila coonadi?

Nyimbo 16 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani