LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 8/15 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 10

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 10
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA AUGUST 10
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 8/15 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa August 10

MLUNGU WA AUGUST 10

Nyimbo 61 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 13 ndime 19-23, ndi bokosi pa tsa. 137 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Mafumu 21-22 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Mafumu 22:13-23 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Mungayandikile Bwanji Mulungu?—igw-CIN tsa. 28 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: Delila—Mutu: Kukonda Kwambili Ndalama Kungacititse Munthu Cinyengo—w12 4/15 tsa. 8 ndime 4 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Koma ine ndi a m’nyumba yanga, tizitumikila Yehova.”—Yoswa 24:15.

Nyimbo 41

Mph. 10: “Koma Ine ndi a m’Nyumba Yanga, Tizitumikila Yehova.” Nkhani yozikidwa pa lemba la mwezi. Ŵelengani ndi kufotokoza Deuteronomo 6:6, 7; Yoswa 24:15; ndi Miyambo 22:6. Gogomezelani kuti amuna afunika kutsogolela banja lao pa zinthu za kuuzimu. Chulani zida zosiyanasiyana zimene gulu lafalitsa zothandiza mabanja. Chulani nkhani zina za mu Msonkhano wa Nchito za mwezi uno ndipo fotokozani mmene zikugwilizanilana ndi lemba la mwezi.

Mph. 20: “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Phunzitsani Atsopano.” Kukambilana. Pemphani omvela kuti afotokoze mmene makolo angagwilitsile nchito mfundo za m’nkhaniyi pothandiza ana ao kupita patsogolo mwa kuuzimu. Citani citsanzo coonetsa tate akukonzekela ulaliki ndi mwana wake wamng’ono.

Nyimbo 93 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani