LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 March tsa. 5
  • Munthu Wokhulupilika Yobu Afotokoza Mavuto Ake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Munthu Wokhulupilika Yobu Afotokoza Mavuto Ake
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • “Yembekezela Yehova”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Limbikitsani Ena ndi Mau Abwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Kodi Yobu Anali Ndani?
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 March tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YOBU 6-10

Munthu Wokhulupilika Yobu Afotokoza Mavuto Ake

Anzake atatu a Yobu

Yobu anakhala wosauka, wofedwa, ndipo anadwala kwambili, koma anakhalabe wokhulupilika. Conco, Satana anayesa kumufooketsa kuti asiye kukhala wokhulupilika. “Anzake” atatu a pamtima anabwela kwa iye. Poyamba anaonetsa cifundo. Iwo anakhala ndi Yobu kwa masiku 7 osakamba ngakhale mau amodzi omulimbikitsa. Koma mau amene anakamba pambuyo pake, anali omuimba mlandu okhaokha.

Yobu anakhalabe wokhulupilika kwa Yehova ngakhale anakumana ndi mavuto ambili

6:3; 7:16; 9:20-22; 10:1, 12

  • Cisoni cinacititsa Yobu kukhala ndi maganizo olakwika. Iye anaganiza molakwika n’kumaona kuti Mulungu analibe nazo nchito zakuti iye ndi munthu wokhulupilika

  • Cifukwa cofooka ndi mavuto, Yobu sanadziŵe zimene zinali kucititsa mavuto ake

  • Ngakhale kuti Yobu anali ndi cisoni cacikulu, anauza anthu amene anali kumutsutsa kuti iye anali kukonda Yehova

Yobu ali ndi zilonda thupi lonse
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani