LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 March tsa. 8
  • Kalata ya Citsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kalata ya Citsanzo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Moseŵenzetsela Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Kuongolela Luso Lathu mu Ulaliki—Tizilemba Tikapeza Anthu Acidwi
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 March tsa. 8

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kalata ya Citsanzo

  • Seŵenzetsani adresi yanu. Ngati muona kuti si bwino kuseŵenzetsa adresi yanu, mungaseŵenzetse adresi ya Nyumba ya Ufumu, koma mololedwa na akulu. Komabe, SIMUFUNIKA kuseŵenzetsa adresi ya ofesi ya nthambi monga adresi yanu.

  • Lembani dzina la mwininyumbayo ngati mulidziŵa. Mukatelo, munthuyo sangaganize kuti kalatayo ni ya otsatsa malonda.

  • Onetsetsani kuti masipeling’i, ziganizo, komanso zizindikilo zopumila zili bwino. Kalatayo ifunika kukhala yooneka bwino osati yauve. Ngati mwailembela pamanja, ikhale yosavuta kuŵelenga. Mawu a m’kalatayo safunika kukhala opeputsa kapena aulemu kwambili.

Kalata ya citsanzo imene talembayi ionetsa mfundo zimene tafotokoza. Sanailembe n’colinga cakuti muzikopela mawu ake onse mukamalembela munthu wa m’gawo lanu ayi. Lembani kalata yanu mogwilizana n’colinga cake, komanso cikhalidwe ca kumaloko.

Kalata ya Citsanzo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani