LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 May tsa. 5
  • Mungapambane Ngakhale Kuti Muli na “Munga M’thupi”!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mungapambane Ngakhale Kuti Muli na “Munga M’thupi”!
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • “Munga M’thupi” la Paulo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Inu Makolo—Thandizani Ana Anu Kukonda Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Seŵenzetsani Mfundo za m’Baibo Pothandiza Ana Anu Kuti Apambane
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 May tsa. 5
Talita, amayi ake, na mbale wake akutamba vidiyo pa jw.org; amayi ake akumufotokozela zithunzi za m’vidiyoyo

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Mungapambane Ngakhale Kuti Muli na “Munga M’thupi”!

M’masiku otsiliza ovuta ano, mavuto amene ali ngati minga amasautsa atumiki onse a Mulungu. (2 Tim. 3:1) Kodi tingamudalile bwanji Yehova kuti tikwanitse kulimbana nawo mavuto amenewo? Tambitsani vidiyo yakuti “Maso a Anthu Akhungu Adzatseguka,” kuti muone zimene Talita Alnashi na makolo ake anacita. Kenako, yankhani mafunso aya:

  • N’ciani cili ngati “munga m’thupi” kwa Talita?

  • Ni malonjezo a m’Baibo ati amene athandiza Talita na makolo ake kukhalabe acimwemwe?

  • Kodi makolo a Talita anaonetsa bwanji cidalilo cawo pa Yehova pambuyo pa opaleshoni ya Talita?

  • Kodi makolo a Talita anaseŵenzetsa bwanji zofalitsa za gulu pothandiza mwana wawo kukulitsa cikondi cake pa Mulungu?

  • Kodi Talita anaonetsa bwanji kuti akukula mwauzimu olo kuti ali na “munga m’thupi”?

  • Kodi citsanzo ca Talita cakulimbikitsani bwanji?

Talita akamba za ciyembekezo cake, aŵelenga mocita kuseŵenzetsa sikilini, ayankha pa misonkhano, ndipo ali mu ulaliki na atate ake
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani