LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 November tsa. 4
  • Tifunika Kumenya Nkhondo kuti Tikhalebe m’Coonadi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tifunika Kumenya Nkhondo kuti Tikhalebe m’Coonadi
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Analemba za Yesu
    Phunzitsani Ana Anu
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 November tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 YOHANE 1-13; 3 YOHANE 1-14-YUDA 1-25

Tifunika Kumenya Nkhondo kuti Tikhalebe m’Coonadi

Yuda 3

Munthu akuyesetsa mwamphamvu kuti aloŵe pakhomo lopapatiza

Yesu anatiilimbikitsa kuti: “Yesetsani mwamphamvu kuloŵa pakhomo lopapatiza.” (Luka 13:24) Mawu a Yesu aonetsa kuti tifunika kulimbikila, kuyesetsa kuti Mulungu atiyanje. Yuda m’bale wake wa Yesu, anauzilidwa kulemba mawu ofanana na amenewa. Anati: ‘Menyani mwamphamvu nkhondo yacikhulupililo.’ Timafunika kuyesetsa mwakhama kuti tikwanitse kucita zotsatilazi:

  • Kupewa dama.—Yuda 6, 7

  • Kulemekeza amene ali na ulamulilo.—Yuda 8, 9

  • Kudalila kwambili ziphunzitso zozikidwa pa “cikhulupililo . . . coyela kopambana,” kutanthauza ziphunzitso zacikhristu.—Yuda 20, 21

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani