LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsa. 4
  • May 11-17

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • May 11-17
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 May tsa. 4

May 11-17

GENESIS 38-39

  • Nyimbo 33 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Sanamusiye Yosefe”: (10 min.)

    • Gen. 39:1—Yosefe anakhala kapolo ku Iguputo (w14 11/1 12 ¶4-5)

    • Gen. 39:12-14, 20—Yosefe ananamizilidwa na kuikidwa m’ndende (w14 11/1 14-15)

    • Gen. 39:21-23—Yehova anakhalabe naye Yosefe (w14 11/1 15 ¶2)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Gen. 38:9, 10—N’cifukwa ciani Yehova anapha Onani? (it-2 555)

    • Gen. 38:15-18—Kodi ni mfundo ziti zimene tiyenela kumvetsa pa zimene Yuda na Tamara anacita? (w04 1/15 30 ¶4-5)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mbali ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 38:1-19 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi, ndiyeno funsani omvetsela: Kodi mlongo wacita ciani kuti amveketse bwino uthenga wake kwa mwininyumba? (th phunzilo 17) Kodi wofalitsa akanafuna kugaŵilanso cofalitsa ca m’Thuboksi Yathu akanacita bwanji?

  • Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 1)

  • Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Mukayamba makambilano acitsanzo, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki. Koma mwaluso, loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 11)

  • Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo, ndiyeno gaŵilani kakhadi kongenela pa webusaiti yathu. (th phunzilo 6)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 121

  • “Khalani Monga Yosefe—Thaŵani Zaciwelewele”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Thawani Zaciwelewele.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo : (30 min.) jy mutu 114

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 26 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani