LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb24 May masa. 10-11
  • June 10-16

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • June 10-16
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2024
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2024
mwb24 May masa. 10-11

JUNE 10-16

MASALIMO 48-50

Nyimbo 126 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Makolo—Thandizani Banja Lanu Kudalila Kwambili Gulu la Yehova

(Mph. 10)

Thandizani ana anu kumuyandikila Yehova na gulu lake (Sal. 48:​12, 13; w22.03 22 ¶11; w11 3/15 19 ¶5-7)

Phunzitsani ana anu mbili ya gulu la Yehova (w12-CN 8/15 12 ¶5)

Mwa citsanzo canu, phunzitsani ana anu kutsatila malangizo ocokela ku gulu la Yehova (Sal. 48:14)

Zithunzi: 1. Tate akukambilana na mwana wake mfundo ya m’buku lakuti “Gulu Lokhazikitsidwa Kucita Cifunilo ca Yehova.” 2. Banja likutamba JW Broadcasting. 3. Banja lapita kukaona malo osungilako zinthu zakale pa Beteli. 4. Mayi akuseŵenzetsa “Buku Lapachaka la Mboni za Yehova” komanso lakuti “Jehovah’s Witnesses—Proclaimers of God’s Kingdom” pophunzila na mwana wake wamkazi.

ZIMENE MUNGACITE PA KULAMBILA KWA PABANJA: Nthawi na nthawi muzitamba na kukambilana mavidiyo opezeka pa mbali yakuti “Gulu Lathu” pa jw.org.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Sal. 49:​6, 7—Kodi Aisiraeli anayenela kukumbukila ciyani pa zinthu zabwino zimene anali nazo? (it-2-E 805)

  • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutigaŵilako?

3. Kuŵelenga Baibo

(Mph. 4) Sal. 50:​1-23 (th phunzilo 11)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kucotsa Mantha—Mmene Yesu Anacitila Zimenezi

(Mph. 7) Kukambilana. Tambitsani VIDIYO, kenako kambilanani lmd phunzilo 6 mfundo 1-2.

5. Kucotsa Mantha—Tengelani Citsanzo ca Yesu

(Mph. 8) Makambilano ozikika mu lmd phunzilo 6 mfundo 3-5, komanso mbali yakuti “Onaninso Malemba Awa.”

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 73

6. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

7. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 11 ¶1-4, mawu oyamba a cigawo 4, na mabokosi pa mas. 86-87

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 103 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani