LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb24 July tsa. 3
  • July 8-14

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 8-14
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2024
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2024
mwb24 July tsa. 3

JULY 8-14

MASALIMO 60-62

Nyimbo 2 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Zithunzi: 1. Mwamuna akuthamangila ku nsanja yolimba. 2. Mwamuna akumwetulila ndipo akuitanila anthu mu tenti yake mmene muli alendo omwe akudya. 3. Thanthwe lalikulu.

1. Yehova Amatiteteza, Amaticinjiliza, Ndiponso Amatilimbitsa

(Mph. 10)

Yehova ali ngati nsanja yolimba (Sal. 61:3; it-2-E 1118 ¶7)

Yehova amatilola kukhala alendo mu tenti yake (Sal. 61:4; it-2-E 1084 ¶8)

Yehova ali monga thanthwe (Sal. 62:2; w02-CN 4/15 16 ¶14)


DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi umoyo wanga wasintha bwanji n’kukhala wabwino cifukwa codziŵa Yehova na kumudalila?’

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Sal. 62:11—Kodi “mphamvu ndi za Mulungu” m’lingalilo lotani? (w06-CN 6/1 11 ¶8)

  • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuŵelenga Baibo

(Mph. 4) Sal. 60:1–61:8 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Yambitsani makambilano pambuyo pakuti munthu wakuonetsani kukoma mtima. (lmd phunzilo 2 mfundo 3)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) KUNYUMBA NA NYUMBA. Uzani mwini nyumba za JW Library®, ndipo muonetseni mmene angaicitile daunilodi. (lmd phunzilo 7 mfundo 4)

6. Nkhani

(Mph. 5) w22.02 4-5 ¶7-10—Mutu: Khulupililani Yehova Mukalandila Malangizo. (th phunzilo 20)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 12

7. Palibe ‘Cingatilekanitse ndi cikondi ca Mulungu’

(Mph. 10) Kukambilana.

Tambitsani VIDIYO. Kenako funsani omvela kuti:

  • Kodi Yehova anamuthandiza bwanji M’bale Nyirenda pamene anali kuzunzidwa?

8. Khala Bwenzi la Yehova—Zoyenela Kucita Kuti Ubatizike

(Mph. 5) Kukambilana. Tambitsani VIDIYO. Ndiyeno, ngati n’kotheka, pemphani ana amene munaŵasankhilatu kuti abwele ku pulatifomu ndipo afunseni kuti: Ngati ufuna kubatizika, kodi cofunika kwambili n’ciyani kuposa msinkhu wako? Ni zinthu zina ziti zomwe uyenela kucita kuti ubatizike?

9. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 12 ¶7-13, bokosi pa tsa. 97

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 63 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani