LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 March tsa. 3
  • March 10-16

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • March 10-16
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 March tsa. 3

MARCH 10-16

MIYAMBO 4

Nyimbo 36 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Mlonda yemwe ali pa nsanja akuuza alonda a pageti kuti atseke mageti a mzindawo.

Alonda akucitapo kanthu mwamsanga pamene adani akuyandikila mzinda

1. “Uteteze Mtima Wako”

(Mph. 10)

Liwu lakuti “mtima” likutanthauza umunthu wamkati (Sal. 51:6; w19.01 15 ¶4)

Tiyenela kuonetsetsa kuti tikuuteteza mtima wathu (Miy 4:23a; w19.01 17 ¶10-11; 18 ¶14; onani pacikuto)

Kuti tikhale ndi umoyo wabwino zimadalila mmene mtima wathu wophiphilitsa ulili (Miy. 4:23b; w12-CN 5/1 32 ¶2)

M’bale waceukila kumbali kuti asaone zinthu zosayenela zomwe zaonekela pafoni yake.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Miy. 4:18​—Kodi vesiyi imatithandiza bwanji kumvetsa mmene Mkhristu amapitila patsogolo kuuzimu? (w21.08 8 ¶4)

  • Pa kuwelenga Baibulo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibulo

(Mph. 4) Miy. 4:​1-18 (th phunzilo 12)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Munthuyo waonetsa cidwi pambuyo polandila kapepala komuitanila ku Cikumbutso. (lmd phunzilo 1 mfundo 5)

5. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. Itanilani ku Cikumbutso munthu amene mudziwa. (lmd phunzilo 2 mfundo 3)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupilila

(Mph. 5) Citsanzo. ijwfq nkhani 19​—Mutu: N’cifukwa Ciyani a Mboni za Yehova Sakondwelela Isitala? (lmd phunzilo 3 mfundo 4)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 16

7. Vidiyo yakuti Zimene Gulu Lakwanitsa Kucita ya March

(Mph. 10) Tambitsani VIDIYO.

8. Kuitanila Anthu ku Cikumbutso Kudzayamba pa Ciŵelu, March 15

(Mph. 5) Ikambidwe ndi woyang’anila utumiki. Fotokozani makonzedwe a pampingo panu okhudza kampeni, nkhani yapadela, komanso Cikumbutso. Limbikitsani ofalitsa onse kucita zambili muutumiki m’miyezi ya March ndi April.

9. Phunzilo la Baibulo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 23 ¶16-19, bokosi pa tsa. 188

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 76 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani