LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 May tsa. 8
  • May 26–June 1

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • May 26–June 1
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 May tsa. 8

MAY 26–JUNE 1

MIYAMBO 15

Nyimbo 102 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Thandizani Ena Kukhala Acimwemwe

(Mph. 10)

Abale athu akamakumana ndi mavuto aakulu, angamaone monga masiku onse a moyo wawo ndi oipa (Miy. 15:15)

Muzikhala oceleza kwa anthu amene akukumana ndi mavuto (Miy. 15:17; w10-CN 11/15 31 ¶16)

“Kuyang’ana munthu ndi nkhope yacimwemwe” komanso kumuuza mawu ocepa olimbikitsa kungakhale kothandiza kwambili (Miy. 15:​23, 30, mawu a m’munsi; w18.04 23-24 ¶16-18)

Mwamuna ndi mkazi wake akusangalala pamene akudya cakudya ndi mlongo wacikulile kunyumba kwake.

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi ndi ndani mumpingo mwathu amene ndingamulimbikitse? Nanga ndingamuthandize bwanji?’

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Miy. 15:22​—Kodi mfundo ya palembali ingatithandize bwanji kupanga zisankho zabwino pa nkhani ya cithandizo ca mankhwala? (ijwbq-CN nkhani 39 ¶3)

  • Pa kuwelenga Baibulo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibulo

(Mph. 4) Miy. 15:​1-21 (th phunzilo 2)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) KUNYUMBA NDI NYUMBA. (lmd phunzilo 1 mfundo 5)

5. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. M’pempheni kuti muziphunzila naye Baibulo. (lmd phunzilo 2 mfundo 4)

6. Kupanga Ophunzila

(Mph. 5) Limbikitsani wophunzila Baibulo amene akutsutsidwa ndi a m’banja lake. (th phunzilo 4)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 155

7. Tingakhalebe Acimwemwe Ngakhale Pamene Tikukumana ndi Mavuto

(Mph. 15) Kukambilana.

Tambitsani VIDIYO yakuti Tingakhalebe Okondwela Ngakhale pa Zowawa, Njala, Komanso pa Usiwa. Kenako, funsani omvela kuti:

  • Kodi mwaphunzilapo ciyani pa zocitika za mu vidiyo iyi?

8. Phunzilo la Baibulo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 27 ¶1-9

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 100 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani