LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 May tsa. 9
  • June 2-8

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • June 2-8
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 May tsa. 9

JUNE 2-8

MIYAMBO 16

Nyimbo 36 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Mafunso Atatu Amene Angatithandize Kupanga Zisankho Zabwino

(Mph. 10)

Kodi ndimadalila malangizo a Yehova? (Miy. 16:​3, 20; w14 1/15 19-20 ¶11-12)

Kodi cisankho canga cidzakondweletsa Yehova? (Miy. 16:7)

Kodi ndimatengela kwambili zimene anthu ena amakamba kapena kucita? (Miy. 16:25; w13 9/15 17 ¶1-3)

M’bale wacinyamata ali mu sitolo yogulitsa zovala, ndipo wogulitsa akumuonetsa suti yothina. M’baleyo akufunsa ngati angapeze suti ina yoyenelela.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi mafunso awa angandithandize bwanji kupanga zisankho zabwino pa nkhani ya kavalidwe ndi kudzikongoletsa?’

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Miy. 16:22​—Kodi “zitsilu zimalangidwa ndi kupusa kwawo komwe” m’njila yotani? (it-1-E 629)

  • Pa kuwelenga Baibulo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibulo

(Mph. 4) Miy. 16:​1-20 (th phunzilo 12)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Onetsani munthu mmene webusaiti ya jw.org ingamuthandizile. (lmd phunzilo 2 mfundo 5)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Pemphani munthu amene anakanapo kuphunzila Baibulo kuti muziphunzila naye. (lmd phunzilo 9 mfundo 5)

6. Nkhani

(Mph. 5) ijwbv nkhani 40​—Mutu: Kodi Miyambo 16:3 itanthauza ciyani? (th phunzilo 8)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 32

7. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

8. Phunzilo la Baibulo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 27 ¶10-18

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 68 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani