LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 May tsa. 14
  • June 23-29

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • June 23-29
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 May tsa. 14

JUNE 23-29

MIYAMBO 19

Nyimbo 154 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Khalani Bwenzi Lenileni kwa Abale Anu

(Mph. 10)

Muzinyalanyaza zolakwa zawo (Miy. 19:11; w23.11 12-13 ¶16-17)

Muziwathandiza pa nthawi ya mavuto (Miy. 19:17; w23.07 9-10 ¶10-11)

Muziwaonetsa cikondi cosasintha (Miy. 19:22; w21.11 9 ¶6-7)

Cithunzi ca gulu la abale na alongo akumwetulila.

CITSANZO: Tingayelekezele zinthu zimene timakumbukila ndi zithunzi. Timasunga zithunzi zabwino zokhazokha. Mofananamo, tizikumbukila zabwino zokhazo zimene abale athu amacita.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Miy. 19:17​—N’cifukwa ciyani kuthandiza anthu onyozeka kuli monga kukongoza Yehova? (w87-CN 5/15 29)

  • Pa kuwelenga Baibulo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibulo

(Mph. 4) Miy. 19:​1-20 (th phunzilo 2)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Popanda kukamba coonadi ca m’Baibulo, cezani ndi munthuyo m’njila yoti adziwe kuti ndinu wa Mboni za Yehova, ndipo m’pempheni kuti muziphunzila naye Baibulo. (lmd phunzilo 2 mfundo 4)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. Pa makambilano apita, munthuyo anakuuzani kuti amakonda zacilengedwe. (lmd phunzilo 9 mfundo 4)

6. Nkhani

(Mph. 5) lmd zakumapeto A mfundo 10​—Mutu: Mulungu Ali Ndi Dzina. (th phunzilo 20)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 40

7. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

8. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 28 ¶1-7

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 61 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani