LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 July tsa. 10
  • August 4-10

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • August 4-10
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 July tsa. 10

AUGUST 4-10

MIYAMBO 25

Nyimbo 154 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yesu akulankhula m’sunagoge atanyamula mpukutu wotsegula. Gulu la amuna, akazi, ndi ana akumvetsela mwachelu.

Yesu ali m’sunagoge ku Nazareti, ndipo anthu akudabwa ndi mawu ake ogwila mtima

1. Malangizo Anzelu Otithandiza Kuti Tizilankhula Bwino

(Mph. 10)

Muzisankha nthawi yabwino yolankhula (Miy. 25:11; w15-CN 12/15 19 ¶6-7)

Muzilankhula mokoma mtima komanso mwaubwenzi (Miy. 25:15; w15-CN 12/15 21 ¶15-16; onani cithunzi)

Muzilankhula mawu olimbikitsa (Miy. 25:25; w95-CN 4/1 17 ¶8)

Mlongo wacitsikana akulankhula mwaulemu ndi aphunzitsi ake.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Miy. 25:28​—Kodi mwambi uwu utanthauza ciyani? (g19.3 6 ¶3)

  • Pa kuwelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibo

(Mph. 4) Miy. 25:​1-17 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Yambani kukambilana ndi munthu amene akuoneka wosakondwa. (lmd phunzilo 3 mfundo 3)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Munthuyo wakuuzani kuti ali ndi cipembedzo cake ndipo sangasinthe. (lmd phunzilo 8 mfundo 4)

6. Nkhani

(Mph. 5) ijwyp nkhani 23​—Mutu: Kodi Ndingatani Ngati Anthu Ena Amakonda Kunena za Ine? (th phunzilo 13)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 123

7. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

8. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) rr mutu 1 ¶15-19 ndi bokosi 1B

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 15 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani