LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 November tsa. 9
  • December 1-7

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • December 1-7
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 November tsa. 9

DECEMBER 1-7

YESAYA 3-5

Nyimbo 135 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Panali Poyenela Yehova Kuyembekezela Kuti Anthu Ake Azimumvela

(Mph. 10)

Yehova “anabzala munda wake wa mpesa” ndi kuusamalila bwino, ndipo anali kuyembekezela kuti udzabeleka zipatso zabwino (Yes. 5:​1, 2, 7; ip-1-CN 73-74 ¶3-5; 76 ¶8-9)

Munda wa Yehova wa “mpesa” unangobeleka zipatso za m’chile (Yes. 5:4; w06-CN 6/15 18 ¶1)

Yehova analonjeza kuti adzausiya mundawo kuti ukhale wosalimidwa (Yes. 5:​5, 6; w06-CN 6/15 18 ¶2)

Mlimi wakhumudwa poona kuti mphesa zimene anabzala m’munda wake sizinacite bwino.

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi nkhani imeneyi indilimbikitsa bwanji kupewa kukhumudwitsa Yehova?’

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Yes. 5:​8, 9​—Kodi Aisiraeli anali kucita ciyani cimene cinali kukhumudwitsa Yehova? (ip-1-CN 80 ¶18-19)

  • Pa kuwelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibo

(Mph. 4) Yes. 5:​1-12 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Sewenzetsani vidiyo ya mu Thuboksi ya Zida Zophunzitsila. (lmd phunzilo 1 mfundo 5)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. Uzani munthuyo za JW Laibulale, ndipo m’thandizeni kuicita daunilodi pafoni yake. (lmd phunzilo 9 mfundo 5)

6. Kupanga Ophunzila

(Mph. 5) Limbikitsani wophunzila Baibo amene akutsutsidwa ndi a m’banja lake. (lmd phunzilo 12 mfundo 4)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 65

7. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

8. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) rr mutu 7 ¶8-15 ndi bokosi 7A

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 7 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani