LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • g18 na. 2 tsa. 16
  • 12 Zolinga

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • 12 Zolinga
  • Galamuka!—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Malangizo Owonjezela kwa Makolo
    Galamuka!—2019
  • Thandizo Ilipo
    Galamuka!—2020
  • Tingapeze Kuti Mayankho a Mafunso Ofunika Kwambili Onena za Umoyo?
    Tingapeze Kuti Mayankho a Mafunso Ofunika Kwambili Onena za Umoyo?
  • Kulemekezana m’Banja
    Galamuka!—2024
Onaninso Zina
Galamuka!—2018
g18 na. 2 tsa. 16
Wacicepele alemba pulani

Malangizo Owonjezela Ku Mabanja

BAIBO IMAPELEKA CITSOGOZO CODALILIKA KWAMBILI kwa okwatilana, makolo, komanso kwa acicepele. Mfundo zake zingathandize munthu kuwonjezela luso lake la kuganiza na kupanga zosankha zabwino.—Miyambo 1:1-4.

BAIBO IMAYANKHANSO MAFUNSO OFUNIKA KWAMBILI MU UMOYO, MONGA AKUTI:

  • Kodi colinga ca moyo n’ciani?

  • Kodi tiyenela kuimba mlandu Mulungu cifukwa ca mavuto athu?

  • Kodi cimacitika n’ciani munthu akamwalila?

Tikupemphani kuti muziphunzila Baibo pamwekha kuti mupeze mayankho pa mafunso aya komanso ena. Tambani vidiyo yakuti, N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo? Unikani kacidindo ka QR aka kapena yendani pa www. jw. org.

Kuti mudziŵe zambili zokhudza anthu okwatilana komanso umoyo wa banja, yendani pa webusaiti ya jw.org, pa cigawo cakuti, ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA pa webusaiti ya Chichewa. Yendani pa www. jw. org, kapena unikani kacidindo ka QR aka

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani