LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • g21 na. 2 tsa. 15
  • Phunzilani Zambili pa JW.ORG

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Phunzilani Zambili pa JW.ORG
  • Galamuka!—2021
  • Nkhani Zofanana
  • Thandizo Ilipo
    Galamuka!—2020
  • 12 Zolinga
    Galamuka!—2018
  • Pezani Nzelu Zothandiza pa Umoyo pa JW.ORG
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Colinga ca Webu Saiti Yathu Ndi Kuthandiza Ife ndi Anthu Ena
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
Onaninso Zina
Galamuka!—2021
g21 na. 2 tsa. 15

Phunzilani Zambili Pa Jw.Org

Ni nkhani iti imene mungakonde kuiŵelenga?

Mwamuna na mkazi wake akuseŵenzetsa mafoni awo pamene ali mkati mwa kudya.

Zimene mungacite kuti zinthu ziziyenda bwino m’cikwati canu

Onani nkhani ya ku Chichewa yakuti “Kodi Mungatani Kuti Zipangizo Zamakono Zisamakusokonezeni?”

Tate akuphunzitsa mwana wake mmene angaseŵenzetsele foni mwanzelu.

Mmene mungaphunzitsile ana anu makhalidwe abwino

Onani vidiyo ya zithunzi zojambula pamanja yakuti “Kodi Zipangizo Zanu Zimakulamulilani?”

Wa zanyengo akufotokoza mmene nyengo idzayendela m’masiku 7.

Mmene mungacepetsele nkhawa ya zakutsogolo

Onani nkhani zakuti “Kodi Kutsogolo Kuli Ciani?”

Baibo ingakuthandizeni inu na banja lanu kukhala na umoyo wacimwemwe palipano komanso ciyembekezo ca tsogolo labwino.

PA JW.ORG PALINSO: Maphunzilo a Baibo a pa Intaneti. Ni aulele, ndipo simuyenela kucita kulembetsa.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani