LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CO-pgm17 masa. 6-7
  • Tsiku Lacitatu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tsiku Lacitatu
  • Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2017
  • Nkhani Zofanana
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2020
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2022
Onaninso Zina
Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2017
CO-pgm17 masa. 6-7
Zithunzi zoonetsa mfundo zazikulu za tsiku lacitatu kumadzulo, pa msonkhano wacigawo wa Mboni za Yehova.

Tsiku Lacitatu

“Amene adzapilile mpaka pa mapeto, ndiye amene adzapulumuke”—MATEYU 24:13

KUM’MAŴA

  • 8:20 Nyimbo za Pavidiyo

  • 8:30 Nyimbo 83 na Pemphelo

  • 8:40 YOSIILANA: Tifunika ‘Kuthamanga Mopilila’

    • Thamangani Kuti Mupambane! (1 Akorinto 9:24)

    • Konzekelani Mwakhama (1 Akorinto 9:25-27)

    • Tayani Zolemetsa Zosafunika (Aheberi 12:1)

    • Tengelani Zitsanzo Zabwino (Aheberi 12:2, 3)

    • Idyani Zakudya Zopatsa Thanzi (Aheberi 5:12-14)

    • Imwani Madzi Ambili (Chivumbulutso 22:17)

    • Tsatilani Malamulo a Mpikisano (2 Timoteyo 2:5)

    • Khalani na Cidalilo Cakuti Mudzalandila Mphoto (Aroma 15:13)

  • 10:10 Nyimbo 130 na Zilengezo

  • 10:20 NKHANI YA ANTHU ONSE: Musataye Mtima! (Yesaya 48:17; Yeremiya 29:11)

  • 10:50 Cidule ca Nsanja ya Mlonda

  • 11:20 Nyimbo 148 na Kupumula

Zithunzi zoonetsa mfundo zazikulu za tsiku lacitatu kumadzulo, pa msonkhano wacigawo wa Mboni za Yehova.

KUMASANA

  • 12:35 Nyimbo za Pavidiyo

  • 12:45 Nyimbo 142

  • 12:50 SEŴELO: “Kumbukilani Mkazi wa Loti”—Mbali 3(Luka 17:28-33)

  • 13:20 Nyimbo 65 na Zilengezo

  • 13:30 “Uziwayembekezelabe . . . Iwo Sadzacedwa!”(Habakuku 2:3)

  • 14:30 Nyimbo 154 na Pemphelo Lothela

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani