LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 January tsa. 7
  • Yehova Amafuna Anthu Omutumikila Mocita Kufuna Okha

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Amafuna Anthu Omutumikila Mocita Kufuna Okha
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Ezara Aphunzitsa Cilamulo ca Mulungu
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mungakhalebe na Cidalilo mu Nthawi Zovuta
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Khalidwe la Ezara Linacititsa Kuti Yehova Alemekezeke
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Kudalila Thandizo La Mulungu
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 January tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EZARA 6-10

Yehova Amafuna Anthu Omutumikila Mocita Kufuna Okha

Yopulinta
Ayuda akucoka ku Babulo ndi kupita ku Yerusalemu limodzi ndi Ezara

Ezara anakonza zobwelela ku Yerusalemu

7:6, 22; 8:26, 27

  • Ezara aloledwa ndi Mfumu Aritasasta kubwelela ku Yerusalemu kuti akalimbikitsa anthu kuti azilambila Yehova

  • Mfumu ipatsa Ezara “zopempha zake zonse” zokamangila nyumba ya Yehova—golide, siliva, tiligu, vinyo, mafuta, ndi mcele, ndipo zonse zinakwana $100,000,000, madola a ku America, malinga ndi ndalama za masiku ano

Ezara anakhulupilila kuti Yehova adzateteza atumiki Ake

7:13; 8:21-23

  • Ulendo wobwelela ku Yerusalemu unali wovuta

  • Ulendo unali makilomita pafupifupi 1,600 ndipo njilayo inali kudutsa m’madela oopsa

  • Ulendowo unatenga miyezi inai

  • Aisiraeli amene anabwelela anafunika kukhala ndi cikhulupililo colimba, acangu pa kulambila koona, ndi olimba mtima

EZARA ANANYAMULA . . .

Golide ndi siliva wolema kuposa matalente 750, monga kulema kwa njovu zazikulu pafupifupi zitatu

ZOPINGA ZIMENE ANAKUMANA NAZO POBWELELA . . .

Magulu acifwamba, cipululu coopsa, nyama zoopsa

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani