LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 November tsa. 6
  • Khalanibe Achelu ndi Okangalika Kuuzimu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalanibe Achelu ndi Okangalika Kuuzimu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Dalilani Yehova Kuti Mukhalebe na Moyo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Tengelani Citsanzo kwa Aneneli—Habakuku
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Khalanibe Achelu ndi Okangalika Zinthu Zikasintha mu Umoyo Wanu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Yembekezelanibe!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 November tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | NAHUMU 1–HABAKUKU 3

Khalanibe Achelu ndi Okangalika Kuuzimu

Hab. 1:5, 6

Kwa Ayuda, zakuti Ababulo adzaononga dziko lawo mwina zinaoneka zosatheka. Tikutelo cifukwa Ayuda anali kuthandizidwa na Aiguputo, ndipo Aiguputowo anali na mphamvu kuposa Akasidi. Komanso, Ayuda ambili anali kuona kuti n’zosatheka kuti Yehova alole Yerusalemu na kacisi wake kuwonongedwa. Ngakhale n’conco, ulosi unali kudzakwalitsika ndithu, ndipo Habakuku anafunika kuyembekezelabe pokhala wachelu ndiponso wokangalika kuuzimu.

Mneneli Habakuku akhalabe wachelu ndi wokangalika kuuzimu pamene ena acita zoipa

N’ciani cimanitsimikizila kuti mapeto a dzikoli ali pafupi?

Ningakhale bwanji wachelu komanso wokangalika kuuzimu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani