LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 December tsa. 5
  • Muziimba Mosangalala Nyimbo Zotamanda Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muziimba Mosangalala Nyimbo Zotamanda Yehova
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Nyimbo za Ufumu Zimathandiza Kukhala Wolimba Mtima
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nyimbo Zatsopano Zogwilitsila Nchito Polambila
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Mfundo Yothandiza pa Kuŵelenga Kwanu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Muziimba Mosangalala!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 December tsa. 5
Khala Bwenzi la Yehova Nyimbo 84: Kudzipeleka na Mtima Wonse

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Muziimba Mosangalala Nyimbo Zotamanda Yehova

Paulo na Sila anaimba nyimbo zotamanda Yehova pamene anali m’ndende. (Mac. 16:25) Mosakayikila kuimba kunawathandiza kuti apilile. Nanga bwanji ise masiku ano? Nyimbo zimene timaimba polambila, komanso nyimbo zathu zina, zimatitsitsimula na kutithandiza kukhalabe okhulupilika pokumana na mayeselo. Koposa zonse, nyimbozo zimatamanda Yehova. (Sal. 28:7) Timalimbikitsidwa kuti tiziikako pa mtima mawu a nyimbo zina. Kodi munayesapo kucita zimenezi? Pa kulambila kwa pabanja tikhoza kumaimbako nyimbo kuti tidziŵe mawu ake.

TAMBITSANI VIDIYO YAKUTI ANA ATAMANDA YEHOVA M’NYIMBO

, PAMBUYO PAKE, YANKHANI MAFUNSO OTSATILA:

  • Twatsikana tuŵili tukuimba m’situdiyo

    Kodi kuimba nyimbo za Ufumu kumatikhudza bwanji?

  • Mlongo akukonza zinthu poyembekezela ana oimba

    Kodi Dipatimenti ya Audio/Video imakonzekela bwanji nyimbo zokajambula?

  • Banja likuimba nyimbo pa kulambila kwa pabanja

    Kodi makolo na ana awo amakonzekela bwanji nyimbo zokajambula?

  • Ana akuimba pamodzi

    Kodi mumakonda nyimbo ziti? Nanga n’cifukwa ciani mumazikonda?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani