LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsa. 8
  • Yehova Amakwanilitsa Malonjezo Ake Nthawi Zonse

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Amakwanilitsa Malonjezo Ake Nthawi Zonse
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Tingalimbitse Motani Cikhulupililo Cathu pa Lonjezo la Yehova la Dziko Latsopano?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Mulungu Anamucha Mfumukazi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
  • “Tsopano Uona Zimene Ndicite kwa Farao”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • “Ndiwe Mkazi Wokongola m’Maonekedwe Ako”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 February tsa. 8
Sara ali na pathupi pa Isaki; Sara wagwilila mwana wake Isaki pamene akuona Hagara na Isimaeli akucoka kupita m’cipululu.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 20-21

Yehova Amakwanilitsa Malonjezo Ake Nthawi Zonse

21:1-3, 5-7, 10-12, 14

Yehova anadalitsa Abulahamu na Sara cifukwa ca cikhulupililo cawo, powapatsa mwana wamwamuna. M’kupita kwa nthawi, pokhalabe omvela pokumana na mayeselo, anaonetsa cikhulupililo cawo m’malonjezo a Yehova akutsogolo.

Ngati nikhalabe womvela pokumana na mayeselo, kodi nimaonetsa bwanji kuti nimakhulupilila malonjezo a Yehova akutsogolo? Nanga ningalimbitse bwanji cikhulupililo canga?

Zithunzi: Mlongo amene ali m’cipatala akukamba na dokotala za cosankha cake pa nkhani ya magazi, ndipo mwamuna wake na mwana wake akupenyelela. 2. Kagulu ka abale kasonkhana pamodzi m’nyumba pamene apolisi onyamula zida zankhondo aloŵa m’nyumbamo.
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani