LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsa. 3
  • Kodi Ndimwe Wokonzeka?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Ndimwe Wokonzeka?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Khalanibe Wokonzeka m’Ndime Ino Yothela ya “Masiku Otsiliza”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Kodi Mwakonzekela Kukumana na Zacipolowe?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Thandizani Ena Kupilila pa Nthawi Zovuta
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Mmene Tingathandizile Pakagwa Tsoka
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 May tsa. 3
Banja ikuikilatu m’cola zinthu zofunikila pakacitika ngozi yacilengedwe.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kodi Ndimwe Wokonzeka?

Ngati ngozi yacilengedwe ingacitike m’dela lanu, kodi ingakupezeni muli wokonzeka? Zivomezi, mphepo zamkuntho, moto wa m’nkhalango, komanso kusefukila kwa madzi zingacitike mosayembekezeleka, ndipo zingawononge kwambili. Kuwonjezela apo, kuukila kwa zigaŵenga, zipolowe, na matenda oyambukila zingayambe kulikonse, komanso mosayembekezeleka. (Mlal. 9:11) Tisaganize kuti zinthu ngati zimenezi sizingacitike kumene tikhala.

Aliyense wa ife afunika kucitapo kanthu pokonzekela ngozi yacilengedwe. (Miy. 22:3) Ngakhale kuti gulu la Yehova limapelekako thandizo pakacitika ngozi yacilengedwe, aliyense wa ife ali na udindo wokonzekelelatu.—Agal. 6:5.

TAMBITSANI VIDIYO YAKUTI KODI MWAKONZEKELA TSOKA LA ZACILENGEDWE? KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATILAWA:

  • Mwa kuŵelenga Baibo m’bale akukonzekela kuuzimu kaamba ka ngozi yacilengedwe.

    Kodi kukhala paubale wolimba na Yehova kungatithandize bwanji panthawi ya ngozi yacilengedwe?

  • Cola ca zinthu zofunikila, Foni namba, ndiponso foni.

    N’cifukwa ciani m’pofunika . . .

    • • kupitiliza kukambilana na akulu ngozi yacilengedwe isanacitike, pamene ikucitika, kapena pambuyo pakuti yacitika?

    • • kukhala na cola ca zinthu zofunikila?—g17.5 6

    • • kukambilana mitundu ya ngozi zacilengedwe zimene zingacitike, komanso zimene mungacite pa ngozi iliyonse?

  • Zithunzi: Njila zothandizila ena pa nthawi ya ngozi yacilengedwe. 1. M’bale apemphela. 2. Anthu odzipeleka athandizila pamene kwacitika ngozi yacilengedwe. 3. M’bale akuika ndalama mu kabokosi ka zopeleka pa Nyumba ya Ufumu.

    Kodi tingathandize ena m’njila zitatu ziti pamene ngozi yacilengedwe yawacitikila?

KODI MUNGADZIPELEKE?

Pamafunikila anthu ambili othandizila pakacitika ngozi yacilengedwe. Ngati mungakonde kudzipeleka, dziŵitsani akulu mwamsanga.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani