LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 July tsa. 8
  • Khalani Wodzicepetsa Ena Akakutamandani

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalani Wodzicepetsa Ena Akakutamandani
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani Okhulupilika Pamene Mukuyesedwa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yesu Analemekeza Atate Wake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 July tsa. 8

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Khalani Wodzicepetsa Ena Akakutamandani

Nthawi zina, ena angatiyamikile kapena kutitamanda. Izi zingakhale zolimbikitsa ngati zimene anthuwo akamba n’zocokela pansi pa mtima komanso ngati ali na colinga cabwino. (Miy. 15:23; 31:10, 28) Koma tifunika kusamala kuti zimenezo zisatipangitse kudziona wapamwamba, na kuyamba kunyada.

TAMBITSANI VIDIYO YAKUTI KHALANI OKHULUPILIKA MONGA YESU—MUKATAMANDIDWA, NDIYENO YANKHANI MAFUNSO OTSATILAWA:

  • Ni zinthu ziti zimene anthu angatitamande nazo?

  • Kodi abale anam’tamanda bwanji m’bale Seji?

  • Kodi kumutamanda kwawo kunapitilila bwanji pa mlingo woyenela?

  • Muphunzilapo ciani mukaona mmene m’bale Seji anawayankhila modzicepetsa?

Cithunzi ca mu vidiyo yakuti ‘Khalani Okhulupilika Monga Yesu—Mukatamandidwa,’ cikuonetsa Seji ali pamaceza m’nyumba ya m’bale, iye ayankha modzicepetsa pamene abale akumutanda mosayenela.
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani