LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 November tsa. 5
  • Anacita Zinthu Molimba Mtima, Modzipeleka, Komanso Mokangalika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Anacita Zinthu Molimba Mtima, Modzipeleka, Komanso Mokangalika
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Mfumukazi Yoipa Inalangiwa
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • “Nyumba Yonse ya Ahabu Idzafafanizidwa”—2 Maf. 9:8
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Pitilizani Kupempha Citsogozo ca Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Anapilila Zinthu Zopanda Cilungamo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 November tsa. 5
Yehu ali mu galeta lake, ndipo akuuza nduna ya panyumba ya mfumu kuti iponye pansi Yezebeli kucokela pa windo ya nyumba ya nsanjika.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Anacita Zinthu Molimba Mtima, Modzipeleka, Komanso Mokangalika

Yehova analamula Yehu kuti akawononge anthu onse a m’nyumba ya mfumu yoipa Ahabu (2 Maf. 9:6, 7; w11 11/15 3 ¶2)

Mosazengeleza, Yehu anapha Mfumu Yehoramu (mwana wa Ahabu) na Mfumukazi Yezebeli (mkazi wa Ahabu) (2 Maf. 9:22-24, 30-33; w11 11/15 4 ¶2-3; onani chati yakuti “‘Nyumba Yonse ya Ahabu Idzafafanizidwa’—2 Maf. 9:8”)

Yehu anatsiliza nchito imene anapatsidwa, ndipo anaicita molimba mtima, modzipeleka, komanso mokangalika (2 Maf. 10:17; w11 11/15 5 ¶3-4)

DZIFUNSENI KUTI, ‘Ningatengele bwanji citsanzo ca Yehu pogwila nchito imene tinapatsidwa yochulidwa pa Mateyu 28:19, 20?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani