LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 November tsa. 7
  • “Nyumba Yonse ya Ahabu Idzafafanizidwa”—2 Maf. 9:8

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Nyumba Yonse ya Ahabu Idzafafanizidwa”—2 Maf. 9:8
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Mfumukazi Yoipa Inalangiwa
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yezebeli—mfumukazi Yoipa
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Mayi Woipa Komanso Wofunitsitsa Ulamulilo Analangidwa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Anacita Zinthu Molimba Mtima, Modzipeleka, Komanso Mokangalika
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 November tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Nyumba Yonse Ya Ahabu Idzafafanizidwa”—2 Maf. 9:8

“Nyumba Yonse ya Ahabu Idzafafanizidwa.” Chati yoonetsa m’badwo wa mafumu a m’nyumba ya Ahabu.

UFUMU WA YUDA

Yehosafati ni mfumu

ca m’ma 911: Yehoramu (mwana wa Yehosafati, mwamuna wa Ataliya, amene anali mwana wamkazi wa Ahabu na Yezebeli) anayamba kulamulila yekha monga mfumu

ca m’ma 906: Ahaziya (mdzukulu wa Ahabu na Yezebeli) anakhala mfumu

ca m’ma 905: Ataliya anapha ana onse acifumu na kulanda ufumu. M’dzukulu wake Yehoasi ndiye yekha anapulumuka ndipo anabisidwa na Mkulu wa Ansembe Yehoyada.—2 Maf. 11:1-3

ca m’ma 898: Yehoasi anakhala mfumu. Mfumukazi Ataliya anaphedwa na Mkulu wa Ansembe Yehoyada. —2 Maf. 11:4-16

UFUMU WA ISIRAELI

ca m’ma 920: Ahaziya (mwana wa Ahabu na Yezebeli) anakhala mfumu

ca m’ma 917: Yehoramu (mwana wa Ahabu na Yezebeli) anakhala mfumu

ca m’ma 905: Yehu anapha Mfumu Yehoramu ya Isiraeli na abale ake. Anaphanso amayi ake a Yehoramu (Yezebeli) komanso mfumu Ahaziya ya Yuda na abale ake.—2 Maf. 9:14–10:17

ca m’ma 904: Yehu anayamba kulamulila monga mfumu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani