LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 March tsa. 4
  • Tate Apeleka Uphungu Wacikondi kwa Mwana Wake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tate Apeleka Uphungu Wacikondi kwa Mwana Wake
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Thandizani Acinyamata Kuti Apambane
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Kulitsani Cikhumbo Canu Cofuna Kucita Cifunilo ca Mulungu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Moyo wa Munthu Ni Wamtengo Wapatali Kwa Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Thaŵilani kwa Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 March tsa. 4
Zithunzi: 1. Mfumu Davide ili yokalamba ikukambilana na Solomo za pulani ya kamangidwe ka kacisi. 2. Mfumu Solomo ikutsogolela pa nchito yomanga kacisi.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Tate Apeleka Uphungu Wacikondi kwa Mwana Wake

Pa iwe wekha m’dziŵe bwino Yehova (1 Mbiri 28:9; w05 2/15 19 ¶9)

Tumikila Yehova na mtima wathunthu (1 Mbiri 28:9; w12 4/15 16 ¶13)

Dalila Yehova ndipo usacite mantha (1 Mbiri 28:20; w17.09 32 ¶20-21)

Mfumu Davide atakalamba, anapeleka malangizo amenewa kwa mwana wake wacinyamata komanso wosadziŵa zambili, Solomo, asanayambe kugwila nchito yofunika kwambili yomanga kacisi. N’cifukwa ciyani malangizo amenewa ni ofunika kwambili kwa tonsefe, maka-maka kwa Akhristu acinyamata?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani