LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 130
  • Khalani Wokhululuka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalani Wokhululuka
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Muzikhululuka
    Imbirani Yehova
  • “Yehova Anakukhululukilani ndi Mtima Wonse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Yehova Amadalitsa Amene Amakhululukila Anzawo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Tingatengele Bwanji Kukhululuka kwa Yehova?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 130

NYIMBO 130

Khalani Wokhululuka

Yopulinta

(Salimo 86:5)

  1. 1. Atate Yehova,

    Anapeleka Yesu

    Kuti iye atifele,

    Acotsepo na imfa.

    Tikasintha na kulapa,

    Tikasiya zoipa,

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tidzakhululukidwa.

  2. 2. Monga ‘tate wathu,

    Tikhale na cifundo;

    Tikhululukile ena;

    Tionetse cikondi.

    Ticitilane ulemu,

    Ndipo tipililane.

    Ngati tikhululukila

    Tidzakhululukidwa.

  3. 3. Tonse tionetse

    Mkhalidwe wa cifundo.

    Tisadane na abale,

    Tiŵakomele mtima.

    Tikatengela Yehova

    Wopambana m’cikondi,

    Tidzakhululukiladi

    Monga Atate wathu.

(Onaninso Mat. 6:12; Aef. 4:32; Akol. 3:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani