LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsa. 2
  • Yehova Amasamalila Anthu Ake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Amasamalila Anthu Ake
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Muziphunzila Mfundo Zatsopano Mukamaŵelenga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 January tsa. 2

CUMA COCOKELA M’MAU A MULUNGU | YESAYA 24-28

Yehova Amasamalila Anthu Ake

Mofanana ndi munthu wolandila alendo mooloŵa manja, Yehova amatigaŵila cakudya cauzimu ca mwana alilenji.

Cidyelano ca anthu a m’Baibo

“Yehova wa makamu adzakonzela anthu a mitundu yonse . . . phwando la zakudya zabwino zabwino”

25:6

  • M’nthawi za m’Baibo, kudyela pamodzi cakudya kunali kuonetsa kuti anthuwo anali pamtendele ndi paubwenzi

“Zokhala ndi mafuta a m’mafupa, ndiponso la vinyo wokoma kwambili, wosefedwa bwino”

  • Zakudya zabwino-zabwino ndi vinyo wokoma kwambili ziimila zakudya za kuuzimu zabwino ngako zimene Yehova amatipatsa

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani