LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 February tsa. 6
  • Kodi Muli na Maganizo a Ndani?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Muli na Maganizo a Ndani?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Nyamula Mtengo Wako Wozunzikilapo ndi Kunditsatila Mosalekeza
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Kodi Mumayendela Maganizo a Ndani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Tengelani Kaganizidwe ka Yehova ndi Yesu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 February tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MATEYU 16-17

Kodi Muli na Maganizo a Ndani?

16:21-23

Yesu auza Petulo kupita kumbuyo kwake
  • Ngakhale kuti mwina Petulo anali kukamba ali na zolinga zabwino, Yesu sanazengeleze kumuwongolela pa kaganizidwe kake kolakwika.

  • Yesu anadziŵa kuti imeneyo siinali nthawi yakuti ‘adzikomele mtima.’ Mosakayikila, Satana ndiye anali kufuna kuti Yesu adzikomele mtima panthawi yovuta ngati imeneyo.

16:24

Yesu anachula zinthu zitatu zotithandiza kukwanilitsa cifunilo ca Mulungu. Kodi ciliconse ca zinthuzi citanthauza ciani?

  • Kudzikana wekha

  • Kunyamula mtengo wako wozunzikilapo

  • Kutsatila Yesu mosalekeza

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani