LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 73
  • Tilimbitseni Mtima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tilimbitseni Mtima
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tilimbitseni Mtima
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya:
    2018-2019 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woyang’anila Dela
  • Kucotsa Mantha
    Kondani Anthu Kuti Mupange Ophunzila
  • Khalani Wolimba Mtima!
    2018-2019 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woyang’anila Dela
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 73

NYIMBO 73

Tilimbitseni Mtima

Yopulinta

(Machitidwe 4:29)

  1. 1. Pamene tilalikila,

    Uthenga wa Ufumu,

    Ambili amatitsutsa

    Ena amatiseka.

    Koma sitiŵayopa

    Timvelela imwe mwekha

    Conde tipempha mzimu wanu,

    Mvelani pemphelo lathu.

    (KOLASI)

    Tithandizeni Yehova,

    Mu utumiki wathu,

    Tikhale olimba mtima

    Tisayope adani,

    Pamene tiyembekeza

    Tsiku lanu lalikulu,

    Tithandizeni Yehova

    Tipemphela.

  2. 2. Pamene tivutitsiwa,

    Ise mutithandiza,

    Ngakhale ticite mantha

    Imwe mutimvetsetsa.

    Conde tilanditseni

    Kwa adani athu onse.

    Tilankhule molimba mtima

    Pamene tilalikila.

    (KOLASI)

    Tithandizeni Yehova,

    Mu utumiki wathu,

    Tikhale olimba mtima

    Tisayope adani,

    Pamene tiyembekeza

    Tsiku lanu Lalikulu,

    Tithandizeni Yehova

    Tipemphela.

(Onaninso 1 Ates. 2:2; Aheb. 10:35.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani