LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 85
  • Tilandilane Wina Ndi Mnzake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tilandilane Wina Ndi Mnzake
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Landiranani
    Imbirani Yehova
  • Alandileni!
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Alandileni Bwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Landilani Alendo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 85

NYIMBO 85

Tilandilane Wina Ndi Mnzake

Yopulinta

(Aroma 15:7)

  1. 1. Inu nonse takulandilani,

    Mwabwela kuti muphunzile,

    Mau a M’lungu, na njila zake.

    Tiyamike Yehova potiitana.

  2. 2. Tiyamika Atate Yehova,

    Tili na ‘bale acikondi.

    Nthawi zonse amatilandila,

    Tilandile obwela kudzasonkhana.

  3. 3. Yehova afuna anthu onse,

    Aphunzile co’nadi cake.

    Mwa Mwana wake atiitana.

    Tilandile onse mocoka mu’mtima.

(Onaninso Yoh. 6:44; Afil. 2:29; Chiv. 22:17.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani