Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mbiri 12:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma iwo akhala atumiki ake kuti adziwe kusiyana kotumikira ine ndi kutumikira mafumu* a mayiko ena.”

      9 Choncho Sisaki mfumu ya Iguputo anaukira Yerusalemu. Iye anatenga chuma chamʼnyumba ya Yehova+ ndi chuma chamʼnyumba ya mfumu. Anatenga chilichonse kuphatikizapo zishango zagolide zimene Solomo anapanga.+

  • Yeremiya 5:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiye akadzafunsa kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani Yehova Mulungu wathu watichitira zinthu zonsezi?’ udzawayankhe kuti, ‘Mofanana ndi mmene munandisiyira nʼkukatumikira mulungu wachilendo mʼdziko lanu, mudzatumikiranso alendo mʼdziko limene si lanu.’”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani