1 Mafumu 8:66 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 66 Tsiku lotsatira,* Solomo anauza anthuwo kuti azipita, ndipo anthuwo anadalitsa mfumuyo nʼkumapita kwawo. Anapita akusangalala, ali ndi chimwemwe mumtima chifukwa cha zabwino zonse+ zimene Yehova anachitira Davide mtumiki wake komanso anthu ake Aisiraeli. Salimo 13:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika Salimo 31:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Ubwino wanu ndi wochuluka kwambiri!+ Ubwino umenewu mwasungira anthu amene amakuopani,+Ndipo mwausonyeza kwa anthu amene amathawira kwa inu, pamaso pa anthu onse.+ Yesaya 63:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika Yeremiya 31:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Iwo adzabwera nʼkufuula mosangalala pamwamba pa phiri la Ziyoni.+Nkhope zawo zidzawala chifukwa cha ubwino wa* Yehova.Chifukwa cha mbewu, vinyo watsopano+ ndi mafuta,Ndiponso chifukwa cha ana a nkhosa ndi ana a ngʼombe.+ Iwo adzakhala ngati dimba lothiriridwa bwino+Ndipo sadzakhalanso ofooka.”+
66 Tsiku lotsatira,* Solomo anauza anthuwo kuti azipita, ndipo anthuwo anadalitsa mfumuyo nʼkumapita kwawo. Anapita akusangalala, ali ndi chimwemwe mumtima chifukwa cha zabwino zonse+ zimene Yehova anachitira Davide mtumiki wake komanso anthu ake Aisiraeli.
19 Ubwino wanu ndi wochuluka kwambiri!+ Ubwino umenewu mwasungira anthu amene amakuopani,+Ndipo mwausonyeza kwa anthu amene amathawira kwa inu, pamaso pa anthu onse.+
12 Iwo adzabwera nʼkufuula mosangalala pamwamba pa phiri la Ziyoni.+Nkhope zawo zidzawala chifukwa cha ubwino wa* Yehova.Chifukwa cha mbewu, vinyo watsopano+ ndi mafuta,Ndiponso chifukwa cha ana a nkhosa ndi ana a ngʼombe.+ Iwo adzakhala ngati dimba lothiriridwa bwino+Ndipo sadzakhalanso ofooka.”+