Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 25:13-16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Akasidi anaphwanyaphwanya zipilala zakopa+ zomwe zinali mʼnyumba ya Yehova, zotengera zokhala ndi mawilo+ ndiponso thanki ya kopa yosungira madzi+ zimene zinali mʼnyumba ya Yehova, nʼkutenga kopa wake kupita naye ku Babulo.+ 14 Akasidiwo anatenganso ndowa, mafosholo, zozimitsira nyale, makapu ndi ziwiya zonse zakopa zimene ansembe ankagwiritsa ntchito potumikira mʼkachisi. 15 Mkulu wa asilikali olondera mfumu uja anatenga zopalira moto ndi mbale zolowa, zomwe zinali zagolide+ komanso zasiliva weniweni.+ 16 Koma sanathe kuyeza kulemera kwa kopa wa zipilala ziwiri zija, thanki yosungira madzi ndiponso zotengera zokhala ndi mawilo zimene Solomo anapanga kuti zizigwira ntchito panyumba ya Yehova.+

  • Yeremiya 27:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena zokhudza zipilala,+ thanki ya madzi,*+ zotengera zamawilo+ ndi ziwiya zimene zatsala mumzindawu,

  • Yeremiya 27:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 ‘“Ziwiya zimenezi zidzapita ku Babulo+ ndipo zidzakhala kumeneko mpaka tsiku limene ndidzazikumbukire,” akutero Yehova. “Ndipo ndidzazitenga nʼkuzibwezeretsa pamalo ano.”’”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani