Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 27:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Yehova wandiuza kuti, ‘Upange zomangira komanso magoli ndipo uzivale mʼkhosi mwako. 3 Kenako uzitumize kwa mfumu ya Edomu,+ mfumu ya Mowabu,+ mfumu ya Aamoni,+ mfumu ya Turo+ ndi mfumu ya Sidoni.+ Upatsire amithenga amene abwera ku Yerusalemu kudzaonana ndi Zedekiya mfumu ya Yuda.

  • Ezekieli 32:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Edomu+ ali kumeneko. Kulinso mafumu ake ndi atsogoleri ake onse amene ngakhale kuti anali amphamvu, anaikidwa mʼmanda limodzi ndi anthu amene anaphedwa ndi lupanga. Anthu amenewanso adzagona limodzi ndi anthu osadulidwa+ komanso anthu amene akutsikira kudzenje.*

  • Obadiya 1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Awa ndi masomphenya a Obadiya:*

      Zimene Yehova Ambuye Wamkulu Koposa akunena zokhudza Edomu+ ndi izi:

      “Ife tamva uthenga wochokera kwa Yehova,

      Ndipo nthumwi yatumidwa kwa anthu amitundu ina kukanena kuti:

      ‘Konzekani! Tiyeni tikamenyane naye.’”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani