Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 7
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 7:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:3; Sl 44:2
  • +Eks 33:2; Yos 3:10
  • +Ge 10:15
  • +Ge 10:16
  • +Ge 15:16
  • +Ge 10:19
  • +Yos 11:3
  • +Ge 10:17
  • +1Mb 1:14
  • +De 20:1

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    ‘Dziko Lokoma’, ptsa. 10-11

Deuteronomo 7:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 33:52; Mac 13:19
  • +Le 27:29; De 20:17; Yos 6:17; 10:28
  • +Eks 23:32; 34:15; De 20:16; Owe 2:2

Deuteronomo 7:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 23:12; 1Mf 11:2; Eza 9:2; Ne 10:30

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/1/1989, ptsa. 20-21

Deuteronomo 7:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:16; 1Mf 11:4
  • +De 6:15

Deuteronomo 7:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:13; De 12:2
  • +Eks 23:24; De 12:3; 16:22
  • +Owe 6:25
  • +De 16:21
  • +De 7:25; 12:3

Deuteronomo 7:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:6; De 14:2; Yer 2:3
  • +Eks 19:5; Sl 135:4; Amo 3:2; Mki 3:17

Deuteronomo 7:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:37; 10:15; Sl 105:6; Aro 9:11
  • +De 10:22; Sl 105:12; Yes 51:2

Deuteronomo 7:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 13:14
  • +Eks 6:6; 13:3; Yes 51:10
  • +De 23:5
  • +Ge 22:16; Eks 32:13; De 10:15; Sl 105:9; Lu 1:73

Deuteronomo 7:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:45; De 4:35; Sl 68:20
  • +Yes 49:7; 1Ak 10:13; 2Ak 1:18; Ahe 11:11
  • +Ne 1:5; Da 9:4
  • +Eks 34:7; De 5:10

Deuteronomo 7:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 21:9; 68:2; Miy 2:22; Yes 59:18; Nah 1:2; 2Pe 3:7

Deuteronomo 7:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:32; Yoh 13:17; Yak 1:22

Deuteronomo 7:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:26; De 28:1
  • +Sl 105:8
  • +Mik 7:20; Lu 1:55, 72

Deuteronomo 7:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:25; Miy 10:22
  • +Le 26:9
  • +De 28:4
  • +Le 26:4
  • +Sl 107:38
  • +Ge 13:15

Deuteronomo 7:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 33:29; Sl 115:15; 147:20
  • +Eks 23:26; De 28:11; Sl 127:3

Deuteronomo 7:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:27, 60; Amo 4:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/1991, tsa. 4

Deuteronomo 7:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:2; 20:16; Yos 10:28
  • +Ge 15:16; Le 18:25; De 9:5
  • +Eks 20:3
  • +Eks 23:33; De 12:30; Owe 2:3; Sl 106:36

Deuteronomo 7:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 13:31

Deuteronomo 7:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:29; 31:6; Sl 27:1; Yes 41:10
  • +Eks 14:13; Sl 105:27; 135:8; Mac 13:17

Deuteronomo 7:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 29:3; Ne 9:11
  • +Ne 9:10; Yer 32:20
  • +Eks 13:3
  • +De 11:2
  • +De 4:34
  • +Eks 23:28; Yos 3:10

Deuteronomo 7:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 2:25; Yos 2:9; 24:12
  • +Eks 23:29

Deuteronomo 7:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:17; 1Sa 4:8; Ne 1:5; 9:32
  • +Nu 14:9; Sl 46:5

Deuteronomo 7:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:30

Deuteronomo 7:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 9:3

Deuteronomo 7:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 10:24; 12:1
  • +Eks 17:14; Sl 9:5
  • +De 11:25; Yos 1:5; 23:9; Aro 8:31
  • +Yos 11:14

Deuteronomo 7:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:20; De 12:3; 1Mb 14:12
  • +Yes 30:22
  • +Yos 7:21
  • +De 7:16; Owe 8:27
  • +De 27:15; 29:17

Deuteronomo 7:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 2:22
  • +Le 27:28; De 13:17

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 7:1De 31:3; Sl 44:2
Deut. 7:1Eks 33:2; Yos 3:10
Deut. 7:1Ge 10:15
Deut. 7:1Ge 10:16
Deut. 7:1Ge 15:16
Deut. 7:1Ge 10:19
Deut. 7:1Yos 11:3
Deut. 7:1Ge 10:17
Deut. 7:11Mb 1:14
Deut. 7:1De 20:1
Deut. 7:2Nu 33:52; Mac 13:19
Deut. 7:2Le 27:29; De 20:17; Yos 6:17; 10:28
Deut. 7:2Eks 23:32; 34:15; De 20:16; Owe 2:2
Deut. 7:3Yos 23:12; 1Mf 11:2; Eza 9:2; Ne 10:30
Deut. 7:4Eks 34:16; 1Mf 11:4
Deut. 7:4De 6:15
Deut. 7:5Eks 34:13; De 12:2
Deut. 7:5Eks 23:24; De 12:3; 16:22
Deut. 7:5Owe 6:25
Deut. 7:5De 16:21
Deut. 7:5De 7:25; 12:3
Deut. 7:6Eks 19:6; De 14:2; Yer 2:3
Deut. 7:6Eks 19:5; Sl 135:4; Amo 3:2; Mki 3:17
Deut. 7:7De 4:37; 10:15; Sl 105:6; Aro 9:11
Deut. 7:7De 10:22; Sl 105:12; Yes 51:2
Deut. 7:8Eks 13:14
Deut. 7:8Eks 6:6; 13:3; Yes 51:10
Deut. 7:8De 23:5
Deut. 7:8Ge 22:16; Eks 32:13; De 10:15; Sl 105:9; Lu 1:73
Deut. 7:9Le 26:45; De 4:35; Sl 68:20
Deut. 7:9Yes 49:7; 1Ak 10:13; 2Ak 1:18; Ahe 11:11
Deut. 7:9Ne 1:5; Da 9:4
Deut. 7:9Eks 34:7; De 5:10
Deut. 7:10Sl 21:9; 68:2; Miy 2:22; Yes 59:18; Nah 1:2; 2Pe 3:7
Deut. 7:11De 5:32; Yoh 13:17; Yak 1:22
Deut. 7:12Eks 15:26; De 28:1
Deut. 7:12Sl 105:8
Deut. 7:12Mik 7:20; Lu 1:55, 72
Deut. 7:13Eks 23:25; Miy 10:22
Deut. 7:13Le 26:9
Deut. 7:13De 28:4
Deut. 7:13Le 26:4
Deut. 7:13Sl 107:38
Deut. 7:13Ge 13:15
Deut. 7:14De 33:29; Sl 115:15; 147:20
Deut. 7:14Eks 23:26; De 28:11; Sl 127:3
Deut. 7:15De 28:27, 60; Amo 4:10
Deut. 7:16De 7:2; 20:16; Yos 10:28
Deut. 7:16Ge 15:16; Le 18:25; De 9:5
Deut. 7:16Eks 20:3
Deut. 7:16Eks 23:33; De 12:30; Owe 2:3; Sl 106:36
Deut. 7:17Nu 13:31
Deut. 7:18De 1:29; 31:6; Sl 27:1; Yes 41:10
Deut. 7:18Eks 14:13; Sl 105:27; 135:8; Mac 13:17
Deut. 7:19De 29:3; Ne 9:11
Deut. 7:19Ne 9:10; Yer 32:20
Deut. 7:19Eks 13:3
Deut. 7:19De 11:2
Deut. 7:19De 4:34
Deut. 7:19Eks 23:28; Yos 3:10
Deut. 7:20De 2:25; Yos 2:9; 24:12
Deut. 7:20Eks 23:29
Deut. 7:21De 10:17; 1Sa 4:8; Ne 1:5; 9:32
Deut. 7:21Nu 14:9; Sl 46:5
Deut. 7:22Eks 23:30
Deut. 7:23De 9:3
Deut. 7:24Yos 10:24; 12:1
Deut. 7:24Eks 17:14; Sl 9:5
Deut. 7:24De 11:25; Yos 1:5; 23:9; Aro 8:31
Deut. 7:24Yos 11:14
Deut. 7:25Eks 32:20; De 12:3; 1Mb 14:12
Deut. 7:25Yes 30:22
Deut. 7:25Yos 7:21
Deut. 7:25De 7:16; Owe 8:27
Deut. 7:25De 27:15; 29:17
Deut. 7:26Aro 2:22
Deut. 7:26Le 27:28; De 13:17
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 7:1-26

Deuteronomo

7 “Yehova Mulungu wako akadzakulowetsa m’dziko limene ukupita kukalitenga kukhala lako,+ adzakuchotsera mitundu ikuluikulu.+ Adzakuchotsera Ahiti,+ Agirigasi,+ Aamori,+ Akanani,+ Aperezi,+ Ahivi+ ndi Ayebusi,+ mitundu 7 ikuluikulu ndi yamphamvu kuposa iwe.+ 2 Yehova Mulungu wako adzawapereka ndithu kwa iwe ndipo udzawagonjetse.+ Udzawawononge ndithu+ ndipo usadzachite nawo pangano kapena kuwakomera mtima.+ 3 Usadzachite nawo mgwirizano wa ukwati. Usadzapereke ana ako aakazi kwa ana awo aamuna ndipo usadzatenge ana awo aakazi ndi kuwapereka kwa ana ako aamuna.+ 4 Pakuti adzapatutsa ana ako aamuna kuti asanditsatire ndipo adzatumikira ndithu milungu ina.+ Pamenepo mkwiyo wa Yehova udzakuyakirani ndipo adzakuwonongani ndithu mofulumira.+

5 “Koma inu mudzawachitire zotsatirazi: Mudzagwetse maguwa awo ansembe+ ndi kuphwanya zipilala zawo zopatulika.+ Mudzadule+ mizati yawo yopatulika+ ndi kutentha zifaniziro zawo zogoba.+ 6 Pakuti ndinu anthu oyera kwa Yehova Mulungu wanu.+ Yehova Mulungu wanu anakusankhani kuti mukhale anthu ake, chuma chake chapadera, mwa anthu onse okhala padziko lapansi.+

7 “Sikuti Yehova anakusonyezani chikondi ndi kukusankhani chifukwa chakuti munali ochuluka kuposa mitundu yonse,+ chifukwatu mtundu wanu unali waung’ono mwa mitundu yonse.+ 8 Koma Yehova anakutulutsani ndi dzanja lamphamvu+ kuti akulanditseni m’nyumba yaukapolo,+ m’manja mwa Farao mfumu ya Iguputo, chifukwa chakuti Yehova anakukondani,+ komanso chifukwa chosunga lumbiro lake limene analumbirira makolo anu.+ 9 Ndipo iwe ukudziwa bwino kuti Yehova Mulungu wako ndi Mulungu woona,+ Mulungu wokhulupirika,+ wosunga pangano+ ndiponso wosonyeza kukoma mtima kosatha kwa anthu amene amam’konda ndi kusunga malamulo ake ku mibadwo masauzande,+ 10 koma wobwezera munthu wodana ndi Mulunguyo mwa kumuwononga+ pamasom’pamaso. Sadzazengereza kuwononga munthu amene amadana ndi Mulungu. Adzam’bwezera pamasom’pamaso. 11 Uzisunga malamulo, malangizo ndi zigamulo zimene ndikukupatsa lero, mwa kuzitsatira.+

12 “Ndiyeno mukapitiriza kumvera zigamulo zimenezi ndi kuzisunga,+ Yehova Mulungu wanu adzasunga pangano+ ndi kukusonyezani kukoma mtima kosatha, zimene analumbirira makolo anu.+ 13 Ndipo adzakukondani ndithu, kukudalitsani,+ kukuchulukitsani+ ndi kudalitsa zipatso za mimba yanu+ ndi zipatso za nthaka yanu.+ Adzadalitsa mbewu zanu, vinyo wanu watsopano ndi mafuta anu, ana a ng’ombe zanu ndi ana a nkhosa zanu,+ m’dziko limene analumbirira makolo anu kuti adzakupatsani.+ 14 Inu mudzakhala odalitsika mwa anthu onse.+ Pakati panu sipadzapezeka mwamuna, mkazi kapena chiweto chosabereka.+ 15 Yehova adzakuchotserani matenda onse. Ndipo sadzakugwetserani matenda onse oipa a ku Iguputo amene inu mukuwadziwa,+ koma adzawagwetsera pa onse odana nanu. 16 Muwononge anthu a mitundu yonse amene Yehova Mulungu wanu akuwapereka kwa inu.+ Musawamvere chisoni+ ndipo musatumikire milungu yawo+ chifukwa kuchita zimenezo kudzakutcherani msampha.+

17 “Ukaganiza mumtima mwako kuti, ‘Mitundu iyi yandikulira kwambiri. Ndingathe bwanji kuipitikitsa?’+ 18 Usaiope.+ Nthawi zonse uzikumbukira zimene Yehova Mulungu wako anachitira Farao ndi Iguputo yense.+ 19 Uzikumbukira mayesero aakulu amene maso ako anaona,+ zizindikiro, zozizwitsa+ ndiponso dzanja lamphamvu+ ndi mkono wotambasula+ umene Yehova Mulungu wako anakutulutsa nawo m’dzikolo.+ Umu ndi mmene Yehova Mulungu wako adzachitira ndi anthu a mitundu yonse amene ukuwaopa.+ 20 Yehova Mulungu wako adzachititsanso mantha mitima yawo+ kufikira onse otsala+ ndiponso amene anali kubisala pamaso pako atawonongedwa. 21 Usachite nawo mantha pakuti Yehova Mulungu wako, Mulungu wamphamvu ndi wochititsa mantha,+ ali pakati panu.+

22 “Yehova Mulungu wako adzakankhira mitundu imeneyi kutali ndi iwe, kuichotsa pamaso pako pang’onopang’ono.+ Sadzakulola kuifafaniza mofulumira, kuopera kuti zilombo zakutchire zingakuchulukire ndi kukuwononga. 23 Yehova Mulungu wako adzawaperekadi kwa iwe ndi kuwabalalitsa atasokonezeka kwambiri, kufikira atawonongedwa.+ 24 Adzapereka mafumu awo m’manja mwako,+ ndipo iwe udzafafanize mayina awo padziko lapansi.+ Palibe munthu amene adzaima kutsutsana ndi iwe+ kufikira utawafafaniza.+ 25 Mudzatenthe zifaniziro zogoba za milungu yawo.+ Usadzalakelake siliva ndi golide wawo+ kapena kudzitengera zinthu zimenezi,+ kuopera kuti zingakutchere msampha,+ chifukwa zimenezi ndi zonyansa+ kwa Yehova Mulungu wako. 26 Usabweretse m’nyumba mwako zinthu zonyansa kuti iwenso ungawonongedwe mofanana ndi zinthuzo. Uzinyansidwa nazo kwambiri ndi kuipidwa nazo+ chifukwa zinthu zimenezi ndi zoyenera kuwonongedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena